Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:18 - Buku Lopatulika

Nachokera ku Hazeroti, nayenda namanga mu Ritima.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachokera ku Hazeroti, nayenda namanga m'Ritima.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Hazeroti, nakamanga mahema ao ku Ritima.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Heziroti anakamanga ku Ritima.

Onani mutuwo



Numeri 33:18
3 Mawu Ofanana  

Ndipo atatero anthuwo ananka ulendo wao kuchokera ku Hazeroti, namanga mahema ao m'chipululu cha Parani.


Nachokera ku Kibroti-Hatava, nayenda namanga mu Hazeroti.


Nachokera ku Ritima, nayenda namanga mu Rimoni-Perezi.