Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:17 - Buku Lopatulika

Nachokera ku Kibroti-Hatava, nayenda namanga mu Hazeroti.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachokera ku Kibroti-Hatava, nayenda namanga m'Hazeroti.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Kibroti-Hatava, nakamanga mahema ao ku Haseroti.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Kiburoti-Hataava anakamanga misasa yawo ku Heziroti.

Onani mutuwo



Numeri 33:17
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anatcha malowo dzina lake Kibroti-Hatava; popeza pamenepo anaika anthu osusuka.


Kuchokera ku Kibroti-Hatava anthuwo anayenda kunka ku Hazeroti; nakhala ku Hazeroti.


Nachokera ku Hazeroti, nayenda namanga mu Ritima.