Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:15 - Buku Lopatulika

Ndipo anachokera ku Refidimu, nayenda namanga m'chipululu cha Sinai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anachokera ku Refidimu, nayenda namanga m'chipululu cha Sinai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Refidimu, nakamanga mahema ao ku chipululu cha Sinai.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Refidimu anakamanga ku chipululu cha Sinai

Onani mutuwo



Numeri 33:15
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anachoka ku Elimu, ndi khamu lonse la ana a Israele linalowa m'chipululu cha Sini, ndicho pakati pa Elimu ndi Sinai, tsiku lakhumi ndi chisanu la mwezi wachiwiri atatuluka m'dziko la Ejipito.


Ndipo ana a Israele anayenda monga mwa maulendo ao, kuchokera m'chipululu cha Sinai; ndi mtambo unakhala m'chipululu cha Parani.