Ndipo anachoka ku Elimu, ndi khamu lonse la ana a Israele linalowa m'chipululu cha Sini, ndicho pakati pa Elimu ndi Sinai, tsiku lakhumi ndi chisanu la mwezi wachiwiri atatuluka m'dziko la Ejipito.
Numeri 33:15 - Buku Lopatulika Ndipo anachokera ku Refidimu, nayenda namanga m'chipululu cha Sinai. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Ndipo anachokera ku Refidimu, nayenda namanga m'chipululu cha Sinai. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Adanyamuka ku Refidimu, nakamanga mahema ao ku chipululu cha Sinai. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Atachoka ku Refidimu anakamanga ku chipululu cha Sinai |
Ndipo anachoka ku Elimu, ndi khamu lonse la ana a Israele linalowa m'chipululu cha Sini, ndicho pakati pa Elimu ndi Sinai, tsiku lakhumi ndi chisanu la mwezi wachiwiri atatuluka m'dziko la Ejipito.
Ndipo ana a Israele anayenda monga mwa maulendo ao, kuchokera m'chipululu cha Sinai; ndi mtambo unakhala m'chipululu cha Parani.