Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:13 - Buku Lopatulika

Nachokera ku Dofika, nayenda namanga mu Alusi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachokera ku Dofika, nayenda namanga m'Alusi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Dofika, nakamanga mahema ao ku Alusi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Dofika anakamanga misasa yawo ku Alusi.

Onani mutuwo



Numeri 33:13
2 Mawu Ofanana  

Nachokera ku chipululu cha Sini, nayenda namanga mu Dofika.


Nachokera ku Alusi, nayenda namanga mu Refidimu; kumeneko kunalibe madzi kuti anthu amwe.