Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 32:40 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose anapatsa Makiri mwana wa Manase Giliyadi; ndipo anakhala m'menemo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose anapatsa Makiri mwana wa Manase Giliyadi; ndipo anakhala m'menemo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mose adapatsa Makiri mwana wa Manase dziko la Giliyadi, ndipo Makiriyo adakhala m'dziko limenelo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono Mose anapereka Giliyadi kwa Amakiri, ana a Manase, ndipo anakhala kumeneko.

Onani mutuwo



Numeri 32:40
5 Mawu Ofanana  

Ndi Segubu anabala Yairi, amene anali nayo mizinda makumi awiri mphambu itatu m'dziko la Giliyadi.


Ndipo dziko ili tinalilanda muja; kuyambira ku Aroere, wa ku mtsinje wa Arinoni, ndi dera lina la ku mapiri a Giliyadi, ndi mizinda yake, ndinapatsa Arubeni ndi Agadi.


Gawo la fuko la Manase ndi ili: pakuti anali woyamba wa Yosefe. Makiri mwana woyamba wa Manase, atate wa Giliyadi, popeza ndiye munthu wa nkhondo, anakhala nayo Giliyadi ndi Basani.