Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 32:35 - Buku Lopatulika

Ataroti-Sofani, Yazere, ndi Yogobeha;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ataroti-Sofani, Yazere, ndi Yogobeha;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Atiroti-Sofani, Yazere, Yogobeha,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atiroti-Sofani, Yazeri, Yogibeha,

Onani mutuwo



Numeri 32:35
7 Mawu Ofanana  

Naoloka Yordani, namanga zithando ku Aroere ku dzanja lamanja kwa mzinda uli pakati pa chigwa cha Gadi, ndi ku Yazere;


Pakuti minda ya ku Hesiboni yalefuka, ndi mpesa wa ku Sibima; ambuye a mitundu athyolathyola mitengo yosankhika yake; iwo anafikira ngakhale ku Yazere, nayendayenda m'chipululu; nthambi zake zinatasa, zinapitirira panyanja.


Koma ana a Rubeni ndi ana Gadi anali nazo zoweta zambirimbiri; ndipo anapenyerera dziko la Yazere, ndi dziko la Giliyadi, ndipo taonani, malowo ndiwo malo a zoweta.


Ataroti, ndi Diboni, ndi Yazere, ndi Nimira, ndi Hesiboni, ndi Eleyale, ndi Sibima, ndi Nebo, ndi Beoni,


Ndipo ana a Gadi anamanga Diboni, ndi Ataroti, ndi Aroere;


ndi Betenimura, ndi Beteharani: mizinda ya m'malinga, ndi makola a zoweta.


Ndipo Gideoni anakwerera njira ya iwo okhala m'mahema kum'mawa kwa Noba, ndi Yogobeha, nakantha khamulo popeza khamulo linakhala lokhazikika mtima.