Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 31:4 - Buku Lopatulika

Muwatume kunkhondo a fuko limodzi, chikwi chimodzi, atere mafuko onse a Israele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Muwatume kunkhondo a fuko limodzi, chikwi chimodzi, atere mafuko onse a Israele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mutumize ku nkhondo anthu chikwi chimodzi pa fuko lililonse la Israele.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mutumize ku nkhondoko amuna 1,000 kuchokera ku fuko lililonse la Aisraeli.”

Onani mutuwo



Numeri 31:4
5 Mawu Ofanana  

Asanu a inu adzapirikitsa zana limodzi, ndi zana limodzi la inu adzapirikitsa zikwi khumi; ndi adani anu adzagwa pamaso panu ndi lupanga.


Ndipo Mose ananena ndi anthu, nati, Adzikonzere ena mwa inu zida za nkhondo, alimbane nao Amidiyani, kuwabwezera Amidiyani chilango cha Yehova.


Ndipo anapereka mwa zikwi za Israele, a fuko limodzi chikwi chimodzi, anthu zikwi khumi ndi ziwiri okonzekeratu ndi zankhondo.


Ndipo Yehova anati kwa Gideoni. Anthu ali ndi iwe andichulukira kuti ndipereke Midiyani m'dzanja lao; angadzitame Israele pa Ine, ndi kuti, Dzanja la ine mwini landipulumutsa.


Ndipo Yonatani ananena ndi mnyamata wonyamula zida zake, Tiye tipite ku kaboma ka osadulidwa awa; kapena Yehova adzatigwirira ntchito; pakuti palibe chomletsa Yehova kupulumutsa angakhale ndi ambiri kapena ndi owerengeka.