Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 31:39 - Buku Lopatulika

Ndipo abulu anafikira zikwi makumi atatu ndi mazana asanu; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo makumi asanu ndi limodzi mphambu mmodzi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo abulu anafikira zikwi makumi atatu ndi mazana asanu; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo makumi asanu ndi limodzi mphambu mmodzi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Abulu analipo 30,500, ndipo 61 anali gawo la Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

abulu analipo 30,500 ndipo gawo la Yehova linali 61;

Onani mutuwo



Numeri 31:39
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ng'ombe zidafikira zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi chimodzi; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo makumi asanu ndi awiri mphambu ziwiri.


Ndipo anthu anafikira zikwi khumi ndi zisanu ndi chimodzi; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo anthu makumi atatu mphambu awiri.