Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 29:5 - Buku Lopatulika

ndi tonde mmodzi wa nsembe yauchimo, yakutetezera inu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi tonde mmodzi wa nsembe yauchimo, yakutetezera inu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Muperekenso tonde mmodzi kuti akhale nsembe yochitira mwambo wopepesera machimo anu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Muziperekanso mbuzi yayimuna kuti izikhala nsembe yopepesera machimo anu.

Onani mutuwo



Numeri 29:5
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anatenga malaya ake a Yosefe, napha tonde, naviika malaya m'mwazi wake:


Ndi tonde mmodzi, akhale nsembe yauchimo ya Yehova; aikonze pamodzi ndi nsembe yopsereza yosalekeza, ndi nsembe yake yothira.


ndi tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo, yakutetezera inu.


tonde mmodzi wakutetezera inu.


ndi limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;


pamodzi ndi nsembe yopsereza ya pamwezi, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe yopsereza yosalekeza, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe zake zothira, monga mwa lemba lake, zikhale za fungo lokoma, nsembe yamoto ya Yehova.