Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 29:10 - Buku Lopatulika

limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndiponso wa kilogaramu limodzi pa mwanawankhosa aliyense.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kilogalamu imodzi pa mwana wankhosa aliyense mwa asanu ndi awiriwo.

Onani mutuwo



Numeri 29:10
3 Mawu Ofanana  

ndi atatu a magawo khumi a efa wa ufa wosalala, ikhale nsembe yaufa, wosakaniza ndi mafuta, ndiwo wa ng'ombe iliyonse; ndi awiri a magawo khumi a ufa wosalala, ikhale nsembe yaufa, wosakaniza ndi mafuta, ndiwo wa nkhosa yamphongo imodziyo;


tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo, pamodzi ndi nsembe yauchimo yotetezera, ndi nsembe yopsereza yosalekeza, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe zake zothira.


ndi nsembe yao ya ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, atatu a magawo khumi akhale a ng'ombe, awiri a magawo khumi akhale a nkhosa yamphongo imodziyo;