Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 28:22 - Buku Lopatulika

ndi tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo, yakutetezera inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo, yakutetezera inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Muperekenso tonde mmodzi kuti akhale nsembe yochitira mwambo wopepesera machimo anu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Muziphatikizapo mbuzi yayimuna monga nsembe yopepesera machimo anu.

Onani mutuwo



Numeri 28:22
4 Mawu Ofanana  

Ndipo atulukire guwa la nsembe lokhala pamaso pa Yehova ndi kulichitira chotetezera; natengeko mwazi wa ng'ombeyo, ndi mwazi wa mbuziyo, ndi kuupaka pa nyanga za guwa la nsembe pozungulira.


upereke limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi; uzitero ndi anaankhosa asanu ndi awiri;


Pakuti chimene chilamulo sichinathe kuchita, popeza chinafooka mwa thupi, Mulungu anatumiza Mwana wake wa Iye yekha m'chifanizo cha thupi la uchimo, ndi chifukwa cha uchimo, natsutsa uchimo m'thupi;


koma pokwaniridwa nthawi, Mulungu anatuma Mwana wake, wobadwa ndi mkazi, wobadwa wakumvera lamulo,