Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 28:21 - Buku Lopatulika

upereke limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi; uzitero ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

upereke limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi; uzitero ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndiponso wa makilogaramu limodzi pa mwanawankhosa aliyense.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kilogalamu imodzi pa mwana wankhosa aliyense mwa ana ankhosa asanu ndi awiri aja.

Onani mutuwo



Numeri 28:21
2 Mawu Ofanana  

ndi nsembe yao ya efa wa ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta; mupereke atatu a magawo khumi akhale a ng'ombe, ndi awiri a magawo khumi akhale a nkhosa yamphongo;


ndi tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo, yakutetezera inu.