Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 28:18 - Buku Lopatulika

Tsiku loyamba pali kusonkhana kopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsiku loyamba pali kusonkhana kopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa tsiku loyamba pazikhala msonkhano wopatulika. Musagwire ntchito yotopetsa,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa tsiku loyamba muzichita msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse.

Onani mutuwo



Numeri 28:18
4 Mawu Ofanana  

Ndipo tsiku loyamba kukhale kusonkhana kopatulika, ndi tsiku lachisanu ndi chiwiri kukhalenso kusonkhana kopatulika; pasachitike ntchito masikuwo, zokhazi zakudya anthu onse ndizo muzichita.


Ndipo tsiku lachisanu ndi chiwiri mukhale nako kusonkhana kopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena.


Momwemonso tsiku la zipatso zoyamba, pobwera nayo nsembe ya ufa watsopano kwa Yehova, m'chikondwerero chanu cha Masabata, muzikhala nako kusonkhana kopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena.