Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:36 - Buku Lopatulika

Ndipo mwana wamwamuna wa Sutela ndiye Erani, ndiye kholo la banja la Aerani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mwana wamwamuna wa Sutela ndiye Erani, ndiye kholo la banja la Aerani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo ana aamuna a Sutela anali aŵa: Erani anali kholo la banja la Aerani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zidzukulu za Sutela zinali izi: kuchokera mwa Erani, fuko la Aerani.

Onani mutuwo



Numeri 26:36
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana a Efuremu: Sutela, ndi Beredi mwana wake, ndi Tahati mwana wake, ndi Eleada mwana wake, ndi Tahati mwana wake,


Ana aamuna a Efuremu monga mwa mabanja ao ndiwo: Sutela, ndiye kholo la banja la Asutela; Bekere, ndiye kholo la banja la Abekere; Tahani, ndiye kholo la banja la Atahani.


Iwo ndiwo mabanja a ana a Efuremu monga mwa owerengedwa ao, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu ziwiri kudza mazana asanu. Iwo ndiwo ana aamuna a Yosefe monga mwa mabanja ao.