Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 25:17 - Buku Lopatulika

Sautsa Amidiyani ndi kuwakantha;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Sautsa Amidiyani ndi kuwakantha;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Uŵathire nkhondo Amidiyani, ndiponso uŵaononge

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Amidiyani ndi adani anu ndipo uwaphe,

Onani mutuwo



Numeri 25:17
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Mowabu anati kwa akulu a Midiyani, Tsopano msonkhano uwu udzanyambita zonse zili pozinga pathu, monga ng'ombe zinyambita msipu wa kubusa. Ndipo Balaki mwana wa Zipori anali mfumu ya Mowabu masiku amenewo.


Ndipo Israele anakhala mu Sitimu, ndipo anthu anayamba kuchita chigololo ndi ana aakazi a Mowabu;


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,


popeza akusautsani ndi manyengo ao amene anakunyengani nao; m'chija cha Peori, ndi cha Kozibi, mwana wamkazi wa kalonga wa ku Midiyani, mlongo wao, amene adamupha tsiku la mliri, m'chija cha Peori.


Muubwezere, monganso uwu unabwezera, ndipo muwirikize kawiri, monga mwa ntchito zake; m'chikhomo unathiramo, muuthirire chowirikiza.


Koma ana a Israele anachita choipa pamaso pa Yehova; ndipo Yehova anawapereka m'dzanja la Midiyani zaka zisanu ndi ziwiri.