Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 23:28 - Buku Lopatulika

Ndipo Balaki ananka naye Balamu pamwamba pa Peori, popenyana ndi chipululu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Balaki ananka naye Balamu pamwamba pa Peori, popenyana ndi chipululu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho Balaki adatenga Balamu, napita naye pamwamba pa phiri la Peori loyang'anana ndi chipululu cham'munsi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Balaki anamutengera Balaamu pamwamba pa Peori, poyangʼanana ndi chipululu.

Onani mutuwo



Numeri 23:28
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anadziphatikiza ndi Baala-Peori, nadyanso nsembe za akufa.


atachoka ku Bamoti ku chigwa chili m'dziko la Mowabu, ku mutu wa Pisiga, popenyana ndi chipululu.


Ndipo Balaki anati kwa Balamu, Tiyetu, ndimuke nawe kumalo kwina; kapena kudzakomera pamaso pa Mulungu kuti unditembererere iwo pokhala kumeneko.


Ndipo Balamu anati kwa Balaki, Mundimangire pano maguwa a nsembe asanu ndi awiri, nimundikonzere pano ng'ombe zisanu ndi ziwiri, ndi nkhosa zamphongo zisanu ndi ziwiri.


Pamene Balamu anaona kuti kudakomera pamaso pa Yehova kudalitsa Israele, sanamuke, monga nthawi zina zija, ku nyanga zolodzera, koma anayang'ana nkhope yake kuchipululu.