Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 23:25 - Buku Lopatulika

Ndipo Balaki anati kwa Balamu, Usawatemberera konse, kapena kuwadalitsa konse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Balaki anati kwa Balamu, Usawatemberera konse, kapena kuwadalitsa konse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Balaki adauza Balamu kuti, “Musaŵatemberere, ndipo musaŵadalitse.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Balaki anati kwa Balaamu, “Usawatemberere ndi pangʼono pomwe kapena kuwadalitsa!

Onani mutuwo



Numeri 23:25
3 Mawu Ofanana  

Taonani, anthuwo auka ngati mkango waukazi, nadzitukumula ngati mkango waumuna. Sugonanso kufikira utadya nyama yogwira, utamwa mwazi wa zophedwa.


Koma Balamu anayankha nati kwa Balaki, Sindinakuuzani ndi kuti, Chilichonse achinena Yehova, chomwecho ndizichita?