Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 22:39 - Buku Lopatulika

Ndipo Balamu anamuka ndi Balaki, nafika iwo ku Kiriyati-Huzoti.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Balamu anamuka ndi Balaki, nafika iwo ku Kiriyati-Huzoti.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Balamu adapita limodzi ndi Balaki, nakafika ku Kiriyati-Huzoti.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo Balaamu anapita pamodzi ndi Balaki ku Kiriati-Huzoti.

Onani mutuwo



Numeri 22:39
3 Mawu Ofanana  

Ndipo padzakhala kuti pamene Mowabu adzadzionetsa yekha, ndi kudzitopetsa pamsanje, ndipo kufika kumalo ake oyera kudzapemphera, sadzapindulapo kanthu.


Ndipo Balamu anati kwa Balaki, Taonani, ndafika kwa inu; ngati ndili nayo mphamvu konse tsopano kunena kanthu? Mau amene Mulungu aike m'kamwa mwanga ndiwo ndidzanena.


Pamenepo Balaki anapha ng'ombe ndi nkhosa, natumizira Balamu, ndi akalonga okhala naye.