Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 21:31 - Buku Lopatulika

Chomwecho Israele anakhala m'dziko la Aamori.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chomwecho Israele anakhala m'dziko la Aamori.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero Aisraele adakhala m'dziko la Aamori.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Choncho Aisraeli anakhala mʼdziko la Aamori.”

Onani mutuwo



Numeri 21:31
8 Mawu Ofanana  

ndi Aamori, ndi Akanani, ndi Agirigasi, ndi Ayebusi.


Tinawagwetsa; Hesiboni waonongeka kufikira ku Diboni, ndipo tinawapululutsa kufikira ku Nofa. Ndiwo wakufikira ku Medeba.


Ndipo Mose anatumiza anthu akazonde Yazere, nalanda midzi yake, napirikitsa Aamori a komweko.


Ndipo ndinatuma mavu atsogolere inu, amene anawaingitsa pamaso panu, ndiwo mafumu awiri a Aamori; osati ndi lupanga lako, kapena ndi uta wako ai.