Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 21:17 - Buku Lopatulika

Pamenepo Israele anaimba nyimbo iyi, Tumphuka chitsime iwe; muchithirire mang'ombe;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo Israele anaimba nyimbo iyi, Tumphuka chitsime iwe; muchithirire mang'ombe;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Aisraele adaimba nyimbo iyi yakuti, “Tulutsa madzi ako, chitsime iwe, ife tiŵaimbira nyimbo!

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo Aisraeli anayimba nyimbo iyi: “Tulutsa madzi, chitsime iwe! Chiyimbireni nyimbo,

Onani mutuwo



Numeri 21:17
8 Mawu Ofanana  

Muimbireni, muimbireni zomlemekeza; fotokozerani zodabwitsa zake zonse.


Pamenepo anavomereza mau ake; anaimbira chomlemekeza.


Muimbire Yehova; pakuti wachita zaulemerero; chidziwike ichi m'dziko lonse.


chitsime adakumba mafumu, adachikonza omveka a anthu; atanena mlamuli, ndi ndodo zao. Ndipo atachoka kuchipululu anamuka ku Matana;


Kodi wina wa inu akumva zowawa? Apemphere. Kodi wina asekera? Aimbire.


Ndipo Debora ndi Baraki mwana wa Abinowamu anaimba tsiku lomwelo ndi kuti,