Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 2:33 - Buku Lopatulika

Koma sanawerenge Alevi mwa ana a Israele; monga Yehova adauza Mose.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma sanawerenge Alevi mwa ana a Israele; monga Yehova adauza Mose.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Alevi sadaŵaŵerengere kumodzi ndi Aisraele, monga momwe Chauta adaalamulira Mose.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Alevi sanawawerenge pamodzi ndi Aisraeli enawo monga momwe Yehova analamulira Mose.

Onani mutuwo



Numeri 2:33
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ana a Israele anachita monga mwa zonse Yehova adauza Mose, momwemo anamanga mahema ao pa mbendera zao, momwemonso anayenda paulendo, yense monga mwa mabanja ake, monga mwa nyumba za makolo ake.