Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 18:14 - Buku Lopatulika

Zilizonse zoperekedwa chiperekere mu Israele ndi zako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Zilizonse zoperekedwa chiperekere m'Israele ndi zako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chinthu chilichonse chimene anthu amapatulira Chauta m'dziko la Israele chikhale chanu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Chilichonse mu Israeli chomwe chapatulidwira Yehova ndi chako.

Onani mutuwo



Numeri 18:14
4 Mawu Ofanana  

Azidya nsembe yaufa, ndi nsembe yauchimo, ndi nsembe yopalamula; ndipo zilizonse zoperekedwa chiperekere mu Israele ndi zao.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,


koma potuluka m'chaka choliza lipenga, mundawo ukhale wopatulikira Yehova, ngati munda woperekedwa chiperekere kwa Mulungu; ukhale wakewake wa wansembe.


Koma asachigulitse kapena kuchiombola chinthu choperekedwa chiperekere kwa Mulungu, chimene munthu achipereka chiperekere kwa Yehova, chotengako ku zonse ali nazo, ngakhale munthu, kapena nyama, kapena munda wakewake; chilichonse choperekedwa chiperekere kwa Mulungu nchopatulika kwambiri.