Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 16:50 - Buku Lopatulika

Ndipo Aroni anabwera kwa Mose ku khomo la chihema chokomanako; ndi mliri unaleka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Aroni anabwera kwa Mose ku khomo la chihema chokomanako; ndi mliri unaleka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake Aroni adabwerera kwa Mose ku chipata cha chihema chamsonkhano, mliriwo utaleka.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Aaroni anabwerera kwa Mose ku khomo la tenti ya msonkhano, chifukwa mliriwo unali utatha.

Onani mutuwo



Numeri 16:50
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose ndi Aroni anadza kukhomo kwa chihema chokomanako.


Koma akufa nao mliri ndiwo zikwi khumi ndi zinai mphambu mazana asanu ndi awiri, osawerenga aja adafera chija cha Kora.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,