Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 16:20 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anawuza Mose ndi Aaroni kuti,

Onani mutuwo



Numeri 16:20
3 Mawu Ofanana  

Koma nyumba ya Israele inapandukira Ine m'chipululu, sanayende m'malemba anga, nanyoza maweruzo anga, amene munthu akawachita adzakhala nao ndi moyo; ndi masabata anga anawaipsa kwambiri; pamenepo ndidati ndiwatsanulire ukali wanga m'chipululu kuwatha.


Ndipo Kora anasonkhanitsa khamu lonse mopikisana nao ku khomo la chihema chokomanako; ndipo ulemerero wa Yehova unaoneka kwa khamu lonse.


Dzipatuleni pakati pa khamu lino, kuti ndiwathe m'kamphindi.