Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 15:37 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo



Numeri 15:37
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo khamu lonse linamtulutsa kunja kwa chigono, ndi kumponya miyala, ndipo anafa; monga Yehova adauza Mose.


Nena ndi ana a Israele, nuwauze kuti adziombere mphonje m'mphepete mwa zovala zao, mwa mibadwo yao, naike pamphonje m'mphepetemo thonje lamadzi.


Ndipo kumene konse adalowa Iye m'midzi, kapena m'mizinda, kapena kumadera, anthu anagoneka odwala pamisika, nampempha Iye kuti akakhudze ngakhale mphonje yokha ya chovala chake; ndipo onse amene anamkhudza anachiritsidwa.


Mudzipangire mphonje pangodya zinai za chofunda chanu chimene mudzifunda nacho.