Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 14:38 - Buku Lopatulika

Koma Yoswa mwana wa Nuni, ndi Kalebe mwana wa Yefune, anakhala ndi moyo mwa amuna aja adamukawo kukazonda dziko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Yoswa mwana wa Nuni, ndi Kalebe mwana wa Yefune, anakhala ndi moyo mwa amuna aja adamukawo kukazonda dziko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma mwa anthu amene adapita kukazonda dziko aja, Yoswa mwana wa Nuni ndi Kalebe mwana wa Yefune ndiwo adatsala amoyo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mwa anthu amene anakaona dzikolo, Yoswa mwana wa Nuni ndi Kalebe mwana wa Yefune ndi okhawo amene anapulumuka.

Onani mutuwo



Numeri 14:38
5 Mawu Ofanana  

Wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.


amuna amene anaipsa mbiri ya dziko, anafa ndi mliri pamaso pa Yehova.


Ndipo Mose anauza ana a Israele mau onse awa; ndipo anthu anamva chisoni chambiri.


Popeza Yehova adanena za iwowa, Adzafatu m'chipululu. Ndipo sanatsalire mmodzi wa iwowa koma Kalebe mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni.