Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 14:20 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova anati, Ndakhululukira monga mwa mau ako:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova anati, Ndakhululukira monga mwa mau ako:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adati, “Ndaŵakhululukira chifukwa cha mau ako.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anayankha kuti, “Ndawakhululukira monga wapemphera.

Onani mutuwo



Numeri 14:20
7 Mawu Ofanana  

Potero Iye adati awaononge, pakadapanda Mose wosankhika wake, kuima pamaso pake pogamukapo, kubweza ukali wake ungawaononge.


Munawayankha, Yehova Mulungu wathu: munawakhalira Mulungu wakuwakhululukira, mungakhale munabwezera chilango pa zochita zao.


Ndipo Yehova analeka choipa adanenachi, kuwachitira anthu ake.


Koma Mose anati kwa Farao, Ulemu ndi wanu, wa ine ai; ndipembere inu ndi anyamata anu ndi anthu anu liti, kuti aonongeke achulewo, achokere inu ndi nyumba zanu, atsale m'mtsinje mokha?


Atero Yehova, Anthu opulumuka m'lupanga anapeza chisomo m'chipululu; Israele, muja anakapuma.


Chifukwa chake muvomerezane wina ndi mnzake machimo anu, ndipo mupempherere wina kwa mnzake kuti muchiritsidwe. Pemphero la munthu wolungama likhoza kwakukulu m'machitidwe ake.