Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 11:35 - Buku Lopatulika

Kuchokera ku Kibroti-Hatava anthuwo anayenda kunka ku Hazeroti; nakhala ku Hazeroti.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kuchokera ku Kibroti-Hatava anthuwo anayenda kunka ku Hazeroti; nakhala ku Hazeroti.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kuchokera ku Mandaankhuliko, anthu adapita ku Hazeroti, ndipo adakhala komweko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kuchoka pa Kibiroti Hatava anthuwo anayenda kupita ku Heziroti ndipo anakhala kumeneko kwa kanthawi.

Onani mutuwo



Numeri 11:35
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anatcha malowo dzina lake Kibroti-Hatava; popeza pamenepo anaika anthu osusuka.


Ndipo atatero anthuwo ananka ulendo wao kuchokera ku Hazeroti, namanga mahema ao m'chipululu cha Parani.


Nachokera ku Kibroti-Hatava, nayenda namanga mu Hazeroti.


Awa ndi mau amene Mose ananena kwa Israele wonse, tsidya la Yordani m'chipululu, m'chidikha cha pandunji pa Sufu, pakati pa Parani, ndi Tofele, ndi Labani, ndi Hazeroti, ndi Dizahabu.