Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:26 - Buku Lopatulika

Ndi pa gulu la fuko la ana a Asere anayang'anira Pagiyele mwana wa Okarani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi pa gulu la fuko la ana a Asere anayang'anira Pagiyele mwana wa Okarani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtsogoleri wa gulu la fuko la Asere anali Pagiyele mwana wa Okarani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pagieli mwana wa Okirani ndiye anali mtsogoleri wa fuko la Aseri,

Onani mutuwo



Numeri 10:26
4 Mawu Ofanana  

Wa Asere, Pagiyele mwana wa Okarani.


Pamenepo anayenda a mbendera ya chigono cha ana a Dani, ndiwo a m'mbuyombuyo a zigono zonse, monga mwa magulu ao; ndi pa gulu lake anayang'anira Ahiyezere mwana wa Amisadai.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Nafutali anayang'anira Ahira mwana wa Enani.


Tsiku la khumi ndi limodzi kalonga wa ana a Asere, ndiye Pagiyele mwana wa Okarani;