Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 7:44 - Buku Lopatulika

Oimbira: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi anai kudza asanu ndi atatu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Oimbira: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi anai kudza asanu ndi atatu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Oimba nyimbo anali aŵa: a banja la Asafu 148.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.

Onani mutuwo



Nehemiya 7:44
4 Mawu Ofanana  

a ana a Asafu: Zakuri, ndi Yosefe, ndi Netaniya, ndi Asarela, ana a Asafu; mwa chilangizo cha Asafu, wakunenera mwa chilangizo cha mfumu.


Oimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.


A Levi: ana a Yesuwa, a Kadimiyele, a ana a Hodeva, makumi asanu ndi awiri kudza anai.


Odikira: ana a Salumu, ana a Atere, ana a Talimoni, ana a Akubu, ana a Hatita, ana a Sobai, zana limodzi mphambu makumi atatu kudza asanu ndi atatu.