Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 7:41 - Buku Lopatulika

Ana a Pasuri, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ana a Pasuri, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

A banja la Pasuri 1,247.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247

Onani mutuwo



Nehemiya 7:41
6 Mawu Ofanana  

wachisanu Malikiya, wachisanu ndi chimodzi Miyamini,


ndi Adaya mwana wa Yerohamu, mwana wa Pasuri, mwana wa Malikiya, ndi Maasai mwana wa Adiyele, mwana wa Yazera, mwana wa Mesulamu, mwana wa Mesilemiti, mwana wa Imeri,


Ndi a ana a Pasuri: Eliyoenai, Maaseiya, Ismaele, Netanele, Yozabadi, ndi Elasa.


Ana a Pasuri, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.


Ana a Imeri, chikwi chimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.


Ana a Harimu, chikwi chimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.