Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 7:40 - Buku Lopatulika

Ana a Imeri, chikwi chimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ana a Imeri, chikwi chimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

A banja la Imara 1,052.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zidzukulu za Imeri 1,052

Onani mutuwo



Nehemiya 7:40
5 Mawu Ofanana  

wakhumi ndi chisanu Biliga, wakhumi ndi chisanu ndi chimodzi Imeri,


Ana a Imeri, chikwi chimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.


Potsatizana nao anakonza Zadoki mwana wa Imeri pandunji pa nyumba yake. Ndi potsatizana naye anakonza Semaya mwana wa Sekaniya, wosunga Chipata cha Kum'mawa.


Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.


Ana a Pasuri, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.