Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 7:39 - Buku Lopatulika

Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ansembe anali aŵa: a banja la Yedaya, ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa, 973.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973

Onani mutuwo



Nehemiya 7:39
5 Mawu Ofanana  

Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.


Awa tsono ndi akulu a dziko okhala mu Yerusalemu; koma m'midzi ya Yuda yense anakhala pa cholowa chake m'midzi mwao, ndiwo Israele, ansembe, ndi Alevi, ndi antchito a m'kachisi, ndi ana a akapolo a Solomoni.


Ana a Senaa, zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi anai kudza makumi atatu.


Ana a Imeri, chikwi chimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.