Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 7:31 - Buku Lopatulika

Amuna a ku Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Amuna a ku Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amuna a ku Mikimasi 122.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu a ku Mikimasi 122

Onani mutuwo



Nehemiya 7:31
6 Mawu Ofanana  

Anthu a Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.


Amuna a ku Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.


Amuna a ku Betele ndi Ai, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza atatu.


Wafika ku Ayati, wapitirira kunka ku Migironi; pa Mikimasi asunga akatundu ake;


Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anatuluka kunja ku mpata wa ku Mikimasi.


Ndipo Afilisti anasonkhana kuti akamenyane ndi Aisraele, anali nao magaleta zikwi makumi atatu, ndi apakavalo zikwi zisanu ndi chimodzi, ndi anthu akuchuluka monga mchenga wa m'mphepete mwa nyanja. Iwowa anakwera namanga zithando ku Mikimasi kum'mawa kwa Betaveni.