Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 7:30 - Buku Lopatulika

Amuna a ku Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Amuna a ku Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amuna a ku Rama ndi Geba, 621.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu a ku Rama ndi Geba 621

Onani mutuwo



Nehemiya 7:30
6 Mawu Ofanana  

Ana a Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.


Ana a Benjamini omwe, kuyambira ku Geba pa Mikimasi, ndi Aya, ndi pa Betele ndi midzi yake,


ndi ku Betegiligala, ndi ku minda ya Geba ndi Azimaveti; popeza oimbirawo adadzimangira midzi pozungulira Yerusalemu.


Amuna a ku Kiriyati-Yearimu, Kefira, ndi Beeroti, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi anai kudza atatu.


Amuna a ku Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.