Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 7:27 - Buku Lopatulika

Amuna a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Amuna a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amuna a ku Anatoti 128.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu a ku Anatoti 128

Onani mutuwo



Nehemiya 7:27
6 Mawu Ofanana  

Anthu a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.


Amuna a ku Betelehemu ndi ku Netofa, zana limodzi mphambu makumi asanu ndi atatu kudza asanu ndi atatu.


Amuna a ku Betazimaveti, makumi anai kudza awiri.


Fuula ndi mau ako iwe mwana wamkazi wa Galimu! Tamva, iwe Laisa! Iwe Anatoti wosauka!


Mau a Yeremiya mwana wa Hilikiya, wa ansembe amene anali ku Anatoti m'dziko la Benjamini;


Chifukwa chake atero Yehova za anthu a Anatoti, amene afuna moyo wanga, kuti, Usanenere m'dzina la Yehova, ungafe ndi mkono wathu;