Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 6:5 - Buku Lopatulika

Pamenepo Sanibalati anatuma mnyamata wake kwa ine kachisanu, ndi kalata yosatseka m'dzanja mwake;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo Sanibalati anatuma mnyamata wake kwa ine kachisanu, ndi kalata wosatseka m'dzanja mwake;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo Sanibalati adatumanso wantchito wake kachisanu kwa ine. Iye anali ndi kalata yosamata m'manja mwake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono kachisanu, Sanibalati anatumiza wantchito wake ndi kalata yosamata.

Onani mutuwo



Nehemiya 6:5
7 Mawu Ofanana  

Nanditumizira ine mau otere kanai; ndinawabwezeranso mau momwemo.


m'menemo mudalembedwa, Kwamveka mwa amitundu, ndi Gesemu achinena, kuti iwe ndi Ayuda mulikulingirira za kupanduka; chifukwa chake mulikumanga lingali; ndipo iwe udzakhala mfumu yao monga mwa mau awa.


kuti asatichenjerere Satana; pakuti sitikhala osadziwa machenjerero ake.


Tavalani zida zonse za Mulungu, kuti mudzakhoze kuchilimika pokana machenjerero a mdierekezi.


ndi m'chinyengo chonse cha chosalungama kwa iwo akuonongeka, popeza chikondi cha choonadi sanachilandire, kuti akapulumutsidwe iwo.