Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 3:22 - Buku Lopatulika

Ndi potsatizana naye anakonza ansembe okhala kuchidikha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi potsatizana naye anakonza ansembe okhala kuchidikha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambali pa Meremoti, ansembe okhala ku chidikha adakonza chigawo china.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pambuyo pake ansembe okhala ku chidikha anakonzanso chigawo china.

Onani mutuwo



Nehemiya 3:22
4 Mawu Ofanana  

Ana a oimbirawo anasonkhana ochokera ku dziko lozungulira Yerusalemu, ndi kumidzi ya Anetofa,


Potsatizana naye Meremoti mwana wa Uriya mwana wa Hakozi anakonza gawo lina, kuyambira kukhomo la nyumba ya Eliyasibu kufikira malekezero ake a nyumba ya Eliyasibu.


Potsatizana nao anakonza Benjamini ndi Hasubu pandunji pa nyumba pao. Potsatizana nao anakonza Azariya mwana wa Maaseiya mwana wa Ananiya pafupi pa nyumba yake.


anatumiza mau kwa ine Sanibalati ndi Gesemu, kuti, Tiyeni tikomane kumidzi ya ku Chigwa cha Ono; koma analingirira za kundichitira choipa.