Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 12:9 - Buku Lopatulika

Ndi Bakibukiya ndi Uni, abale ao, anawayang'anira maulonda.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi Bakibukiya ndi Uni, abale ao, anawayang'anira maulonda.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Abale ao, Bakibukiya ndi Uni, ankaimba molandizana nawo pa nthaŵi ya chipembedzo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Abale awo, Bakibukiya ndi Uri, ankayimba nyimbo molandizana.

Onani mutuwo



Nehemiya 12:9
4 Mawu Ofanana  

Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliyasibu ndi Eliyasibu anabala Yoyada,


Ndi akulu a Alevi: Hasabiya, Serebiya, ndi Yesuwa mwana wa Kadimiyele, ndi abale ao openyana nao, kulemekeza ndi kuyamika, monga mwa lamulo la Davide munthu wa Mulungu, alonda kupenyana alonda.


Ndi Alevi ndiwo Yesuwa, Binuyi, Kadimiyele, Serebiya, Yuda, ndi Mataniya; iye ndi abale ake amatsogolera mayamiko.