Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliyasibu ndi Eliyasibu anabala Yoyada,
Nehemiya 12:9 - Buku Lopatulika Ndi Bakibukiya ndi Uni, abale ao, anawayang'anira maulonda. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Ndi Bakibukiya ndi Uni, abale ao, anawayang'anira maulonda. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Abale ao, Bakibukiya ndi Uni, ankaimba molandizana nawo pa nthaŵi ya chipembedzo. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Abale awo, Bakibukiya ndi Uri, ankayimba nyimbo molandizana. |
Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliyasibu ndi Eliyasibu anabala Yoyada,
Ndi akulu a Alevi: Hasabiya, Serebiya, ndi Yesuwa mwana wa Kadimiyele, ndi abale ao openyana nao, kulemekeza ndi kuyamika, monga mwa lamulo la Davide munthu wa Mulungu, alonda kupenyana alonda.
Ndi Alevi ndiwo Yesuwa, Binuyi, Kadimiyele, Serebiya, Yuda, ndi Mataniya; iye ndi abale ake amatsogolera mayamiko.