Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 12:21 - Buku Lopatulika

wa Hilikiya, Hasabiya; wa Yedaya, Netanele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

wa Hilikiya, Hasabiya; wa Yedaya, Netanele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Wa fuko la Hilikiya anali Hasabiya ndipo wa fuko la Yedaya anali Netanele.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

wa fuko la Hilikiya anali Hasabiya; wa fuko la Yedaya anali Netaneli.

Onani mutuwo



Nehemiya 12:21
4 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene adaitana mfumu, anawatulukira Eliyakimu mwana wa Hilikiya woyang'anira nyumba ya mfumu, ndi Sebina mlembi, ndi Yowa mwana wa Asafu wolemba mbiri.


wa Salai, Kalai; wa Amoki, Eberi;


M'masiku a Eliyasibu, Yoyada, Yohanani, ndi Yaduwa, Alevi analembedwa akulu a nyumba za makolo; ansembe omwe, mpaka ufumu wa Dariusi wa ku Persiya.


Wa Isakara, Netanele mwana wa Zuwara.