Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 12:13 - Buku Lopatulika

wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanani;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanani;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Wa fuko la Ezara anali Mesulamu, wa fuko la Amariya anali Yehohanani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

wa fuko la Ezara anali Mesulamu; wa fuko la Amariya anali Yehohanani;

Onani mutuwo



Nehemiya 12:13
5 Mawu Ofanana  

Pasuri, Amariya, Malikiya,


Mesulamu, Abiya, Miyamini,


Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe aakulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;


wa Maluki, Yonatani; wa Sebaniya, Yosefe;


Ndipo Ezara mlembi anaima pa chiunda cha mitengo adachimangira msonkhanowo; ndi pambali pake padaima Matitiya, ndi Sema, ndi Anaya, ndi Uriya, ndi Hilikiya, ndi Maaseiya, kudzanja lamanja lake; ndi kudzanja lamanzere Pedaya, ndi Misaele, ndi Malikiya, ndi Hasumu, ndi Hasibadana, Zekariya, ndi Mesulamu.