Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 12:11 - Buku Lopatulika

ndi Yoyada anabala Yonatani, ndi Yonatani, anabala Yaduwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Yoyada anabala Yonatani, ndi Yonatani, anabala Yaduwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yoyada adabereka Yonatani ndipo Yonatani adabereka Yaduwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yoyada anabereka Yonatani, ndipo Yonatani anabereka Yaduwa.

Onani mutuwo



Nehemiya 12:11
3 Mawu Ofanana  

Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliyasibu ndi Eliyasibu anabala Yoyada,


Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe aakulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;


M'masiku a Eliyasibu, Yoyada, Yohanani, ndi Yaduwa, Alevi analembedwa akulu a nyumba za makolo; ansembe omwe, mpaka ufumu wa Dariusi wa ku Persiya.