Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 11:8 - Buku Lopatulika

Ndi wotsatana naye Gabai, Salai, mazana asanu ndi anai mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi wotsatana naye Gabai, Salai, mazana asanu ndi anai mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Achibale ake anali Gabai ndi Salai. Onse pamodzi analipo 928.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Abale ake anali Gabayi ndi Salaya. Onse pamodzi anali 928.

Onani mutuwo



Nehemiya 11:8
3 Mawu Ofanana  

ndi abale ao monga mwa mibadwo yao mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu kudza asanu ndi mmodzi. Onsewa ndiwo akulu a nyumba za makolo ao m'nyumba za makolo ao.


Ndi ana a Benjamini ndi awa: Salu mwana wa Mesulamu, mwana wa Yoedi, mwana wa Pedaya, mwana wa Kolaya, mwana wa Maaseiya, mwana wa Itiyele, mwana wa Yesaya.


Ndi Yowele mwana wa Zikiri ndiye woyang'anira wao, ndi Yuda mwana wa Hasenuwa ndiye wothandizana naye, poyang'anira mzinda.