Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 11:32 - Buku Lopatulika

pa Anatoti, Nobi, Ananiya,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

pa Anatoti, Nobi, Ananiya,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anatoti, Nobi, Ananiya,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ku Anatoti, Nobu ndi Ananiya,

Onani mutuwo



Nehemiya 11:32
10 Mawu Ofanana  

Ana a Benjamini omwe, kuyambira ku Geba pa Mikimasi, ndi Aya, ndi pa Betele ndi midzi yake,


Hazori, Rama, Gitaimu,


Amuna a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.


Fuula ndi mau ako iwe mwana wamkazi wa Galimu! Tamva, iwe Laisa! Iwe Anatoti wosauka!


Lero lomwe adzaima pa Nobu; agwedezera dzanja lake paphiri la mwana wamkazi wa Ziyoni, phiri la Yerusalemu.


Mau a Yeremiya mwana wa Hilikiya, wa ansembe amene anali ku Anatoti m'dziko la Benjamini;


Anatoti ndi mabusa ake, ndi Alimoni ndi mabusa ake; mizinda inai.


Ndipo Davide anafika ku Nobu kwa Ahimeleki wansembeyo; ndipo Ahimeleki anadza kukomana ndi Davide alikunjenjemera, nanena naye, Muli nokha bwanji, palibe munthu wina nanu?


Nati Davide kwa Ahimeleki wansembeyo, Mfumu inandilamulira ntchito, ninena nane, Asadziwe munthu aliyense kanthu za ntchito imene ndakutumira ndi kukulamulira; ndipo ndawapanga anyamatawo ku malo akuti.


Ndipo anakantha Nobu ndiwo mzinda wa ansembe ndi lupanga lakuthwa, anthu aamuna ndi aakazi, ana ndi makanda, ng'ombe ndi abulu, ndi nkhosa, ndi lupanga lakuthwa.