Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 11:21 - Buku Lopatulika

Koma antchito a m'kachisi anakhala mu Ofele, ndi Ziha, ndi Gisipa anali oyang'anira antchito a m'kachisi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Anetini anakhala m'Ofele, ndi Ziha, ndi Gisipa anali oyang'anira Anetini.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma anthu otumikira ku Nyumba ya Mulungu ankakhala ku Ofele, mu Yerusalemu, ndipo Ziha ndi Gisipa ankaŵayang'anira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma antchito a ku Nyumba ya Mulungu ankakhala pa phiri la Ofeli, ndipo Ziha ndi Gisipa ndiwo anali kuwayangʼanira.

Onani mutuwo



Nehemiya 11:21
5 Mawu Ofanana  

Okhala m'dziko oyamba tsono, akukhala mwaomwao m'mizinda mwao, ndiwo Israele, ansembe, Alevi, ndi Antchito a m'kachisi.


Anamanga chipata cha kumtunda cha nyumba ya Yehova, ndi pa linga la Ofele anamanga kwakukulu.


Antchito a m'kachisi: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti,


Koma antchito a m'kachisi okhala mu Ofele anakonza kufikira kumalo a pandunji pa Chipata cha Madzi kum'mawa, ndi nsanja yosomphokayo.


Potsatizana naye anakonza Malikiya wina wa osula golide kufikira kunyumba ya antchito a m'kachisi, ndi ya ochita malonda, pandunji pa Chipata cha Hamifikadi, ndi kuchipinda chosanja cha kungodya.