Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 11:10 - Buku Lopatulika

Mwa ansembe: Yedaya mwana wa Yoyaribu, Yakini,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mwa ansembe: Yedaya mwana wa Yoyaribu, Yakini,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ansembe anali aŵa: Yedaya mwana wa Yoyaribu, Yakini,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ansembe anali awa: Yedaya mwana wa Yowaribu; Yakini;

Onani mutuwo



Nehemiya 11:10
9 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Simeoni: Yemuwele ndi Yamini, ndi Ohadi, ndi Yakini, ndi Zohari, ndi Shaulo, mwana wamwamuna wa mkazi wa ku Kanani.


Ndi a ansembe: Yedaya, ndi Yehoyaribu, ndi Yakini,


Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.


Pamenepo ndinatumiza munthu kuitana Eliyezere, Ariyele, Semaya, ndi Elinatani, ndi Yaribu, ndi Elinatani, ndi Natani, ndi Zekariya, ndi Mesulamu, ndiwo akulu; ndi Yoyaribu ndi Elinatani, ndiwo aphunzitsi.


Seraya mwana wa Hilikiya, mwana wa Mesulamu, mwana wa Zadoki, mwana wa Meraiyoti, mwana wa Ahitubi mtsogoleri wa m'nyumba ya Mulungu;


Ndi Yowele mwana wa Zikiri ndiye woyang'anira wao, ndi Yuda mwana wa Hasenuwa ndiye wothandizana naye, poyang'anira mzinda.


ndi wa Yoyaribu, Matenai; wa Yedaya, Uzi;


Semaya, ndi Yoyaribu, Yedaya.


Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.