Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 10:8 - Buku Lopatulika

Maaziya, Biligai, Semaya, ndiwo ansembe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Maaziya, Biligai, Semaya, ndiwo ansembe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Maziya, Biligai ndi Semaya. Ameneŵa ndiwo anali ansembe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Maziya, Biligai ndi Semaya Awa anali ansembe.

Onani mutuwo



Nehemiya 10:8
7 Mawu Ofanana  

Ndi a ana a Harimu: Maaseiya, ndi Eliya, ndi Semaya, ndi Yehiyele, ndi Uziya.


Mesulamu, Abiya, Miyamini,


Ndi Alevi ndiwo Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa ana a Henadadi, Kadimiyele;


wa Biliga, Samuwa; wa Semaya, Yehonatani;


ndi Maaseiya, ndi Semaya, ndi Eleazara, ndi Uzi, ndi Yehohanani, ndi Malikiya, ndi Elamu, ndi Ezere. Ndipo oimbira anaimbitsa Yezeraya ndiye woyang'anira wao.


Potsatizana nao anakonza Zadoki mwana wa Imeri pandunji pa nyumba yake. Ndi potsatizana naye anakonza Semaya mwana wa Sekaniya, wosunga Chipata cha Kum'mawa.