Nehemiya 10:5 - Buku Lopatulika Harimu, Meremoti, Obadiya, Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Harimu, Meremoti, Obadiya, Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Harimu, Meremoti, Obadiya, Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Harimu, Meremoti, Obadiya, |
Ndi pambali pao anakonza Yedaya mwana wa Harumafa, pandunji pa nyumba yake. Ndi pambali pake anakonza Hatusi mwana wa Hasabineya.
Malikiya mwana wa Harimu, ndi Hasubu mwana wa Pahatimowabu, anakonza gawo lina, ndi Nsanja ya Ng'anjo.
Potsatizana naye Meremoti mwana wa Uriya mwana wa Hakozi anakonza gawo lina, kuyambira kukhomo la nyumba ya Eliyasibu kufikira malekezero ake a nyumba ya Eliyasibu.
Ndi pambali pao anakonza Meremoti mwana wa Uriya, mwana wa Hakozi. Ndi pambali pao anakonza Mesulamu mwana wa Berekiya, mwana wa Mesezabele. Ndi pambali pao anakonza Zadoki mwana wa Baana.