Nehemiya 10:14 - Buku Lopatulika Akulu a anthu: Parosi, Pahatimowabu, Elamu, Zatu, Bani, Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Akulu a anthu: Parosi, Pahatimowabu, Elamu, Zatu, Bani, Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Atsogoleri a anthu anali aŵa: Parosi, Pahatimowabu, Elamu, Zatu, Bani, Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Atsogoleri a anthu anali awa: Parosi, Pahati-Mowabu, Elamu, Zatu, Bani, |
Malikiya mwana wa Harimu, ndi Hasubu mwana wa Pahatimowabu, anakonza gawo lina, ndi Nsanja ya Ng'anjo.