Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 10:11 - Buku Lopatulika

Mika, Rehobu, Hasabiya,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mika, Rehobu, Hasabiya,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mika, Rehobu, Hasabiya,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mika, Rehobu, Hasabiya,

Onani mutuwo



Nehemiya 10:11
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Mefiboseti anali ndi mwana wamwamuna wamng'ono, dzina lake ndiye Mika. Ndipo onse akukhala m'nyumba ya Ziba anali anyamata a Mefiboseti.


ndi Hasabiya, ndi pamodzi naye Yesaya wa ana a Merari, abale ake ndi ana ao makumi awiri;


Pamenepo ndinapatula akulu a ansembe khumi ndi awiri, ndiwo Serebiya, Hasabiya, ndi abale ao khumi pamodzi nao,


ndi abale ao: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,


Zakuri, Serebiya, Sebaniya,


Ndi mwa Alevi: Semaya mwana wa Hasubu, mwana wa Azirikamu, mwana wa Hasabiya, mwana wa Buni;


Ndipo woyang'anira wa Alevi mu Yerusalemu ndiye Uzi mwana wa Bani, mwana wa Hasabiya, mwana wa Mataniya, mwana wa Mika; mwa ana a Asafu oimbira ena anayang'anira ntchito ya m'nyumba ya Mulungu.


Ndi akulu a Alevi: Hasabiya, Serebiya, ndi Yesuwa mwana wa Kadimiyele, ndi abale ao openyana nao, kulemekeza ndi kuyamika, monga mwa lamulo la Davide munthu wa Mulungu, alonda kupenyana alonda.